Leviticus 6:28 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndipo auphwanye mphika wadothi umene adaphikamo nyamayo. Koma akaphika wamkuŵa, autsuke mphikawo ndi kuutsukuluza ndi madzi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo mphika wadothi umene anaphikamo nyamayi auswe, koma ngati anaiphika mu mphika wamkuwa, atsuke uwu, nautsukuluze ndi madzi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mʼphika wadothi umene aphikira nyamayo auphwanye. Koma ngati yaphikidwa mu mʼphika wa mkuwa, awukweche ndi kuwutsukuluza ndi madzi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo mphika wadothi umene anaphikamo nyamayi auswe, koma ngati anaiphika mu mphika wamkuwa, atsuke uwu, nautsukuluze ndi madzi.