Leviticus 8:35 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Muzikhala pa khomo la chihema chamsonkhano usiku ndi usana, masiku asanu ndi aŵiri, ndipo muzichita zimene Chauta wakulamulani, kuti mungafe. Zimenezi nzimene Chauta wandilamula.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo mukhale pakhomo pa chihema chokomanako masiku asanu ndi awiri, usana ndi usiku, ndi kusunga chilangizo cha Yehova, kuti mungafe; pakuti anandiuza kotero.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Muzikhala pa khomo la tenti ya msonkhano usana ndi usiku kwa masiku asanu ndi awiri. Ndipo muzichita zimene Yehova wakulamulani kuti musafe, pakuti zimenezi ndi zomwe Yehova wandilamulira.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo mukhale pakhomo pa cihema cokomanako masiku asanu ndi awiri, usana ndi usiku, ndi kusunga cilangizo ca Yehova, kuti mungafe; pakuti anandiuza kotero.