Luke 1:12 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zakariya adadzidzimuka pomuwona, nachita mantha.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Zekariya anadabwa pamene anamuona, ndipo mantha anamgwira.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Zakariya ataona mngeloyo, anadzidzimuka ndipo anagwidwa ndi mantha.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Zakariya anadabwa pamene anamuona, ndipo mantha anamgwira.