Luke 1:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Iwo adalemba zimene adaatisimbira anthu oziwona chamaso kuyambira pachiyambi pake, nakhala akuzilalika.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
monga anazipereka kwa ife iwo amene anakhala mboni ndi atumiki a mau,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
monga mmene zinaperekedwera kwa ife ndi iwo amene anaona poyambirira ndi atumiki a mawu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
monga anazipereka kwa ife iwo amene anakhala mboni ndi atumiki a mau,