Luke 1:30 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mngeloyo adamuuza kuti, “Musaope, Maria, Mulungu wakukomerani mtima.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo mngelo anati kwa iye, Usaope, Maria; pakuti wapeza chisomo ndi Mulungu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma mngeloyo anati kwa iye, “Usachite mantha Mariya, pakuti wapeza chisomo pamaso Mulungu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo mngelo anati kwa iye, Usaope, Mariya; pakuti wapeza cisomo ndi Mulungu.