Luke 1:51 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Wachita zamphamvu ndi dzanja lake, wabalalitsa anthu a mtima wonyada.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Iye anachita zamphamvu ndi mkono wake; Iye anabalalitsa odzitama ndi mlingaliro wa mtima wao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye wachita zamphamvu ndi dzanja lake; Iye anabalalitsa iwo amene ali onyada mʼmaganizo awo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Iye anacita zamphamvu ndi mkono wace; 6 Iye anabalalitsa odzitama ndi mlingaliro wa mtima wao,