Luke 1:62 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono adalankhula ndi bambo wake ndi manja, namufunsa kuti, “Mukufuna kuti timutche dzina lanji?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anakodola atate wake, afuna amutche dzina liti?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamenepo anapanga zizindikiro kwa abambo ake kuti adziwe dzina limene akanakonda kumutcha mwanayo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anakodola atate wace, afuna amuche dzina liti?