Luke 1:74 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
kuti adzatipulumutsa kwa adani athu, kuti tizimtumikira mopanda mantha,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kutipatsa ife kuti titalanditsidwa kudzanja la adani athu, tidzamtumikira Iye, opanda mantha,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
kutilanditsa ife mʼdzanja la adani athu, ndi kutipanga ife timutumikire Iye mopanda mantha,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kutipatsa ife kuti titalanditsidwa ku dzanja la adani athu, 17 Tidzamtumikira iye, opanda mantha,