Luke 1:78 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mulungu wathu ndi wa chifundo chachikulu, adzatitumizira kuŵala kwa dzuŵa lam'maŵa kuchokera Kumwamba.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
chifukwa cha mtima wachifundo wa Mulungu wathu. M'menemo mbandakucha wa kumwamba udzatichezera ife.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
chifukwa cha chifundo chachikulu cha Mulungu wathu, ndipo kuwala kwa dzuwa kudzafikira ife kuchokera kumwamba,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa ca mtima wacifundo wa Mulungu wathu. M'menemo mbanda kuca wa kumwamba udzaticezera ife;