Luke 1:79 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kuŵala kwake kudzaunikira onse okhala mu mdima wabii ngati wa imfa, kudzatitsogolera pa njira ya mtendere.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kuwalitsira iwo okhala mumdima ndi mthunzi wa imfa; kulunjikitsa mapazi athu mu njira ya mtendere.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
kuwalira iwo okhala mu mdima ndi mu mthunzi wa imfa, kutsogolera mapazi athu mu njira yamtendere.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
22 Kuwalitsira iwo okhala mumdima ndi mthunzi wa imfa; Kulunjikitsa mapazi athu mu njira ya mtendere.