Luke 11:21 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Munthu wamphamvu akamalonda nyumba yake ali ndi zida zankhondo, katundu wake amakhala pabwino.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamene paliponse mwini mphamvu alonda pabwalo pake zinthu zake zili mumtendere;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Munthu wamphamvu, amene ali ndi zida, akamalondera nyumba yake, katundu wake amatetezedwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamene pali ponse mwini mphamvu alonda pabwalo pace zinthu zace ziri mumtendere;