Luke 11:35 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chenjera tsono kuti kuŵala kumene kuli mwa iwe kusasanduke mdima.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Potero yang'anira kuunika kuli mwa iwe kungakhale mdima.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Onetsetsani tsono, kuti kuwunika kuli mwa inu si mdima.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Potero yang'anira kuunika kuli mwa iwe kungakhale mdima.