Luke 12:34 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pajatu kumene kuli chuma chako, mtima wakonso kokhala nkomweko.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti kumene kuli chuma chanu, komweko kudzakhalanso mtima wanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Popeza kumene kuli chuma chanu, mtima wanunso udzakhala komweko.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti kumene kuli cuma canu, komweko kudzakhalanso mtima wanu.