Luke 14:13 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma iwe ukamakonza phwando, uziitana amphaŵi, otsimphina, opunduka ndi akhungu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma pamene ukonza phwando uitane aumphawi, opunduka, otsimphina, akhungu;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma ukakonza phwando, itana anthu osauka, ofa ziwalo, olumala ndi osaona.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma pamene ukonza phwando uitane aumphawi, opunduka, otsimphina, akhungu;