Luke 14:35 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ulibenso ntchito ngakhale pa munda, kapena pa dzala. Amangoutaya basi. Amene ali ndi makutu akumva, amve!”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Suyenera kuuthira pamunda kapena padzala, autaya kunja. Amene ali nao makutu akumva amve.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Suyeneranso ngakhale mʼnthaka kapena kudzala la manyowa; umatayidwa kunja. “Amene ali ndi makutu akumva, amve.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Suyenera kuuthira pamunda kapena padzala, autaya kunja. Amene ali nao makutu akumva amve.