Luke 16:29 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma Abrahamu adati, ‘Iwo ali ndi mabuku a Mose ndi a aneneri. Amvere zam'menemo.’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma Abrahamu anati, Ali ndi Mose ndi aneneri; amvere iwo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Abrahamu anayankha kuti, ‘Ali ndi Mose ndi Aneneri; aleke amvere iwo.’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma Abrahamu anati, Ali ndi Mose ndi aneneri; amvere iwo.