Luke 18:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adati, “M'mudzi mwina mudaali woweruza wina amene sankaopa Mulungu kapena kulabadako za munthu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
nanena, M'mudzi mwakuti munali woweruza wosaopa Mulungu, ndi wosasamala munthu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye anati, “Mʼmudzi wina munali woweruza wosaopa Mulungu ngakhalenso kulabadira za anthu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
nanena, M'mudzi mwakuti munali woweruza wosaopa Mulungu, ndi wosasamala munthu.