Luke 18:21 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu uja adati, “Zonsezi ndakhala ndikuzitsata kuyambira ndili mwana.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma anati, Izi zonse ndazisunga kuyambira ubwana wanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye anati, “Zonsezi ndinasunga kuyambira ndili mnyamata.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma anati, Izi zonse ndazisunga kuyambira ubwana wanga.