Luke 18:9 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yesu adaŵapheranso fanizo anthu ena amene ankadziyesa olungama nkumanyoza anzao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anatinso kwa ena amene anadzikhulupirira mwa iwo okha kuti ali olungama, napeputsa onse ena, fanizo ili,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yesu ananena fanizoli kwa amene amadzikhulupirira mwa iwo okha kuti anali wolungama nanyoza ena onse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anatinso kwa ena amene anadzikhulupirira mwa iwo okha kuti ali olungama, napeputsa onse ena, fanizo ili,