Luke 19:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kudafika munthu wina, dzina lake Zakeyo. Iyeyo anali mkulu wa okhometsa msonkho, ndipo anali wolemera.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo taonani, mwamuna wotchedwa dzina lake Zakeyo; ndipo iye anali mkulu wa amisonkho, nali wachuma.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kunali munthu kumeneko dzina lake Zakeyu; iye anali mkulu wa wolandira msonkho ndipo anali wolemera.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndipo Iye anali mkulu wa amisonkho, nali wacuma.