Luke 2:17 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamene adamuwona, abusawo adaŵafotokozera zimene mngelo uja adaaŵauza za mwanayo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo iwo, m'mene anaona, anadziwitsa anthu za mau analankhulidwa kwa iwo a mwana uyu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamene anamuona Iye, iwo anafotokoza zomwe anawuzidwa za mwanayo,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo iwo, m'mene anaona, anadziwitsa anthu za mau analankhulidwa kwa iwo a mwana uyu.