Luke 2:18 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Onse amene ankamva, ankadabwa ndi zimene abusawo ankaŵasimbira.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anthu onse amene anamva anazizwa ndi zinthu abusa adalankhula nao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
ndipo onse amene anamva zimene abusawa ananena anadabwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anthu onse amene anamva anazizwa ndi zinthu abusa adalankhula nao.