Luke 2:19 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma Maria adasunga zonsezo namazilingalira mumtima mwake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma Maria anasunga mau awa onse, nawalingalira mumtima mwake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma Mariya anasunga zonsezi mu mtima mwake ndi kumazilingalira.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma Mariya anasunga mau awa onse, nawalingalira mumtima mwace.