Luke 2:29 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Ambuye, tsopano mundilole ine mtumiki wanu, ndipite ndi mtendere, pakuti mwachitadi zija mudaalonjezazi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Tsopano, Ambuye, monga mwa mau anu aja, lolani ine, kapolo wanu, ndichoke mumtendere;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Ambuye waulamuliro, monga munalonjeza, tsopano lolani kuti mtumiki wanu apite mu mtendere.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Tsopano, Ambuye, monga mwa mau anu aja, Lolani ine, kapolo wanu, ndicoke mumtendere;