Luke 20:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nyengo yothyola zipatso itafika, munthu uja adatuma wantchito wake kwa alimi aja, kuti akampatsireko zipatso za m'munda muja. Koma alimiwo adammenya, nkumubweza osampatsa kanthu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo pa nyengo ya zipatso anatumiza kapolo wake kwa olima mundawo, kuti ampatseko chipatso cha mundawo; koma olimawo anampanda, nambweza wopanda kanthu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pa nthawi yokolola, iye anatumiza wantchito wake kwa alimi aja kuti amupatseko zina mwa zipatso za munda wamphesawo. Koma alimi aja anamumenya namubweza wopanda kanthu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo pa nyengo ya zipatso anatumiza kapolo wace kwa olima mundawo, kuti ampatseko cipatso ca mundawo; koma olimawo anampanda, nambweza wopanda kanthu.