Luke 20:13 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pambuyo pake mwini munda uja adati, ‘Ndichite chiyani tsopano? Ndidzatuma mwana wanga amene ndimamkonda uja. Mwina mwake iye yekhayu akamchitira ulemu.’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo mwini mundawo anati, Ndidzachita chiyani? Ndidzatuma mwana wanga amene ndikondana naye; kapena akamchitira iye ulemu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Kenaka mwini mundawo anati, ‘Kodi ndichite chiyani? Ndidzatumiza mwana wanga wamwamuna, amene ndimukonda; mwina iwo adzamuchitira ulemu.’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo mwini mundawo anati, Ndidzacita ciani? Ndidzatuma mwana wanga amene ndikondana naye; kapena akamcitira iye ulemu.