Luke 20:34 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yesu adaŵayankha kuti, “Anthu okhala pansi pano amakwatira ndi kukwatiwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Yesu anati kwa iwo, Ana a dziko lapansi akwatira nakwatiwa:
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yesu anayankha kuti, “Anthu a mʼbado uno amakwatira ndi kukwatiwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Yesu anati kwa iwo, Ana a dziko lapansi akwatira nakwatiwa: