Luke 20:39 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Apo ena mwa aphunzitsi a Malamulo adauza Yesu kuti, “Aphunzitsi, mwanena bwino.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo alembi ena anayankha nati, Mphunzitsi, mwanena bwino.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ena mwa aphunzitsi amalamulo anayankha kuti, “Mwanena bwino mphunzitsi!”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo alembi ena anayankha nati, Mphunzitsi, mwanena bwino.