Luke 20:40 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adaatero popeza kuti Asaduki aja sadalimbenso mtima kuti amufunse mafunso ena.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti sanalimbenso mtima kumfunsa Iye kanthu kena.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo panalibe wina amene akanalimba mtima kumufunsa Iye mafunso ena.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti sanalimbanso mtima kumfunsa iye kanthu kena.