Luke 21:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono mudziŵiretu kuti musadzachite kukonzekera mau oti mudzaŵayankhe pamlandupo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chifukwa chake tsimikizani mumtima mwanu, kuti usanafike mlandu musalingirire chimene mudzayankha.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma tsimikizani mtima kuti musadzade nkhawa za momwe mudzadzitchinjirizire.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa cace tsimikizani mumtima mwanu, kuti usanafike mlandu musalingirire cimene mudzayankha.