Luke 21:2 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adaonanso mai wina wamasiye akuponyamo tindalama tiŵiri.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anaona mkazi wina wamasiye waumphawi alikuika momwemo timakobiri tiwiri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye anaonanso mkazi wamasiye wosauka akuyikamo timakopala tiwiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anaona mkazi wina wamasiye waumphawi alikuika momwemo timakobiri tiwiri.