Luke 21:29 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pambuyo pake Yesu adaŵaphera fanizo adati, “Yang'anani mkuyu ndi mitengo ina yonse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ananena nao fanizo; Onani mkuyu, ndi mitengo yonse:
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye anawawuza fanizo ili, “Taonani mtengo wamkuyu ndi mitengo ina yonse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ananena nao fanizo; Onani mkuyu, ndi mitengo yonse: