Luke 21:33 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Thambo ndi dziko lapansi zidzatha, koma mau anga sadzatha mphamvu konse.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kumwamba ndi dziko lapansi zidzapita; koma mau anga sadzapita.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kumwamba ndi dziko lapansi zidzatha, koma mawu anga sadzatha.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kumwamba ndi dziko lapansi zidzapita; koma mau anga sadzapita.