Luke 22:29 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nchifukwa chake, monga Atate anga adandipatsa ufumu, Inenso ndikukupatsani ufumu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndipo Ine ndikuikirani ufumu, monganso Atate wanga anandiikira Ine, kuti mukadye ndi kumwa kugome kwanga mu Ufumu wanga;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo Ine ndikupatsani inu ufumu, monga momwe Atate anga anandipatsiranso Ine,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndipo Ine ndikuikirani ufumu, monganso Atate wanga anandiikira Ine, kuti mukadye ndi kumwa kugome kwanga mu Ufumu wanga;