Luke 22:31 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Simoni, Simoni, chenjera! Mulungu walola Satana kuti akupeteni nonse ngati tirigu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Simoni, Simoni, taona, Satana anafunsa akutengeni kuti akupeteni ngati tirigu;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Simoni, Simoni, Satana wapempha kuti akupete ngati tirigu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Simoni, Simoni, taona, Satana anafunsa akutengeni kuti akupeteni ngati tirigu;