Luke 22:62 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamenepo adatuluka, nakalira kwambiri chifukwa cha chisoni chachikulu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anatuluka, nalira misozi ndi kuwawa mtima.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo iye anapita panja nakalira kwambiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anaturuka, nalira misozi ndi kuwawa mtima.