Luke 22:67 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adamuuza kuti, “Ngati ndiwe Mpulumutsi wolonjezedwa uja, utiwuze mosabisa.” Koma Iye adaŵayankha kuti, “Ngakhale ntakuuzani, simungandikhulupirire konse,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
nanena, Ngati uli Khristu, utiuze. Ndipo anati kwa iwo, Ndikakuuzani, simudzavomereza;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwo anati, “Tiwuze, ngati ndiwe Khristu.” Yesu anayankha kuti, “Ine nditakuwuzani simungandikhulupirire.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anati kwa iwo, Ndikakuuzani, simudzabvomereza;