Luke 23:54 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Linali tsiku la chikonzero, tsiku la Sabata likuti liziyamba kumene.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo panali tsiku lokonzera, ndi Sabata linayandikira.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Linali tsiku lokonzekera ndipo Sabata linatsala pangʼono kuyamba.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo panali tsiku lokonzera, ndi Sabata linayandikira.