Luke 23:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamene Pilato adamva zimenezi, adaŵafunsa kuti, “Kodi munthuyu ndi wa ku Galileya?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma pamene Pilato anamva, anafunsa ngati munthuyu ali Mgalileya.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pakumva zimenezi, Pilato anafunsa ngati munthuyo ndi Mgalileya.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma pamene Pilato anamva, anafunsa ngati munthuyu ali Mgalileya.