Luke 24:15 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Akukambirana choncho nkumafunsana, Yesu mwiniwake adayandikira nkumatsagana nawo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo kunali m'kukambirana kwao ndi kufunsana, Yesu mwini anayandikira, natsagana nao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamenepo Yesu mwini wake anabwera ndi kuyenda nawo pamodzi;
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo kunali m'kukambirana kwao ndi kufunsana, Yesu mwini anayandikira, natsagana nao.