Luke 24:37 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma iwo adadzidzimuka, nkuchita mantha poyesa kuti akuwona mzukwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma anaopsedwa ndi kuchita mantha, nayesa alikuona mzimu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma chifukwa choti anathedwa nzeru ndi kuchita mantha, ankaganiza kuti akuona mzukwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma anaopsedwandi kucita mantha, 1 nayesa alikuona mzimu.