Luke 4:28 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu onse amene anali m'nyumba yamapemphero muja atamva mau ameneŵa, adapsa mtima kwambiri.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo onse a m'sunagogemo anadzala ndi mkwiyo pakumva izi;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu onse mʼsunagogemo anapsa mtima atamva izi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo onse a m'sunagogemo anadzala ndi mkwiyo pakumva izi;