Luke 4:32 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zophunzitsa zake anthu zidaaŵagwira mtima kwambiri, chifukwa ankalankhula moonetsa ulamuliro ngati mwiniwake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
chifukwa mau ake anali ndi ulamuliro.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwo anadabwa ndi chiphunzitso chake chifukwa uthenga wake unali ndi ulamuliro.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
cifukwa mau ace anali ndi ulamuliro.