Luke 5:31 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yesu adaŵayankha kuti, “Anthu amene ali bwino sasoŵa sing'anga ai, koma amene akudwala.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Yesu anayankha, nati kwa iwo, Amene ali olimba safuna sing'anga; koma akudwala ndiwo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yesu anawayankha kuti, “Amene sakudwala safuna singʼanga, koma odwala.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Yesu anayankha, nati kwa iwo, Amene ali olimba safuna sing'anga; koma akudwala ndiwo.