Luke 5:32 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Inetu sindidabwere kudzaitana anthu olungama, koma anthu ochimwa, kuti atembenuke mtima.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Sindinadza Ine kuitana olungama, koma ochimwa kuti atembenuke mtima.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine sindinabwere kudzayitana olungama, koma ochimwa kuti atembenuke mtima.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Sindinadza Ine kuitana olungama, koma ocimwa kuti atembenuke mtima,