Luke 5:33 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu ena adauza Yesu kuti, “Ophunzira a Yohane amasala zakudya kaŵirikaŵiri nkumapemphera, chimodzimodzinso ophunzira a Afarisi. Koma ophunzira anu amangodya ndi kumwa.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo iwo anati kwa Iye, Ophunzira a Yohane amasala kudya kawirikawiri, ndi kuchita mapemphero; chimodzimodzinso iwo a Afarisi; koma anu amangokudya ndi kumwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwo anati kwa Iye, “Ophunzira a Yohane amasala kudya ndi kupemphera kawirikawiri, monganso ophunzira a Afarisi, koma anu amangodya ndi kumwa.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo iwo anati kwa iye, Ophunzira a Yohane amasala kudya kawiri kawiri, ndi kucita mapemphero; cimodzimodzinso iwo a Afarisi; koma anu amangokudya ndi kumwa.