Luke 6:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma akuluakulu aja adakwiya kwambiri, nayamba kukambirana zoti achite naye Yesu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma iwowo anagwidwa misala; nalankhulana wina ndi mnzake kuti amchitire Yesu chiyani.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma iwo anapsa mtima nayamba kukambirana wina ndi mnzake chomwe akanamuchitira Yesu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma iwowo anagwidwa misala; nalankhulana wina ndi mnzace kuti amcitire Yesu ciani.