Luke 6:18 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Iwo adabwera kudzamva mau ake, ndiponso kuti Iye aŵachiritse. Anthu amene ankasautsidwa ndi mizimu yoipa, amenewonso Iye ankaŵachiritsa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndipo ovutidwa ndi mizimu yonyansa anachiritsidwa,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwo anabwera kudzamvetsera ndi kuchiritsidwa ku matenda awo. Osautsidwa ndi mizimu yoyipa anachiritsidwa,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndipo obvutidwa ndi mizimu yonyansa anaciritsidwa,