Luke 6:31 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zomwe mukufuna kuti anthu akuchitireni, inuyo muŵachitire zomwezo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo monga mufuna inu kuti anthu adzakuchitirani inu, muwachitire iwo motero inu momwe.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Inu muwachitire anthu ena, zomwe mukanafuna kuti iwo akuchitireni.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo monga mufuna inu kuti anthu adzakucitirani inu, muwacitire iwo motero inu momwe.