Luke 7:1 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yesu atatsiriza kulankhula zonsezi ndi anthu aja, adapita ku Kapernao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamene Yesu adamaliza mau ake onse m'makutu a anthu, analowa m'Kapernao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yesu atamaliza kunena zonsezi pamaso pa anthu amene ankamvetsera, analowa mu Kaperenawo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamene Yesu adamariza mau ace onse m'makutu a anthu, analowa m'Kapernao.